+265881826104
info@starlightmw.org
Blantyre,
Dec 10 2024
Ngati njira imodzi yochepetsera nkhanza zomwe ana achichepere akukumana nazo m’madela omwe timakhala bungwe la Starlight, mogwirizana ndi Police ya mzinda wa Blantyre ikumema anthu okhala m’madela amu mzindawu kuti adzineneza ku Police anthu omwe akuchitira nkhanza ana omwe amakhala nawo.